2 Mbiri 7:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yehova anaonekera kwa Solomoni usiku, nanena naye, Ndamva pemphero lako, ndadzisankhira malo ano akhale nyumba ya nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yehova anaonekera kwa Solomoni usiku, nanena naye, Ndamva pemphero lako, ndadzisankhira malo ano akhale nyumba ya nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono Chauta adamuwonekera usiku namuuza kuti, “Ndamva pemphero lako, ndipo ndadzisankhira malo ano kuti akhale Nyumba yoperekera nsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehova anamuonekera usiku ndipo anati: “Ine ndamva pemphero lako ndipo ndadzisankhira malo ano kukhala Nyumba yanga yoperekeramo nsembe. Onani mutuwo |