Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 6:9 - Buku Lopatulika

9 koma sudzandimangira nyumba ndiwe, koma mwana wako wakudzatuluka m'chuuno mwako, iyeyo adzalimangira dzina langa nyumbayi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 koma sudzandimangira nyumba ndiwe, koma mwana wako wakudzatuluka m'chuuno mwako, iyeyo adzalimangira dzina langa nyumbayi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Komabe si ndiwe udzamange nyumbayo, koma mwana wako wamwamuna amene udzabale, ndiye amene adzandimangire nyumba yomveketsa dzina langa.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Komatu si iwe amene udzamanga Nyumba ya Mulungu koma mwana wako, mwana amene iwe udzabereke. Iyeyo ndiye amene adzandimangire Nyumba.’

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 6:9
6 Mawu Ofanana  

Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;


Koma Mulungu anati kwa ine, Sudzamangira dzina langa nyumba, popeza ndiwe munthu wa nkhondo wokhetsa mwazi.


Ndipo Yehova wakhazikitsa mau ake adanenawo, pakuti ndinauka ine m'malo mwa Davide atate wanga, ndipo ndikhala pa mpando wachifumu wa Israele monga analonjeza Yehova, ndipo ndamangira dzina la Yehova Mulungu wa Israele nyumbayi.


Koma Yehova anati kwa Davide atate wanga, Popeza unafuna mumtima mwako kulimangira dzina langa nyumba, unachita bwino kuti unatero mumtima mwako;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa