2 Mbiri 6:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Davide atate wanga anafuna mumtima mwake kumangira dzina la Yehova Mulungu wa Israele nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Davide atate wanga anafuna mumtima mwake kumangira dzina la Yehova Mulungu wa Israele nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono mumtima mwake bambo wanga Davide ankaganiza zoti amange nyumba yomveketsa dzina la Chauta, Mulungu wa Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Abambo anga Davide anali ndi maganizo mu mtima mwawo oti amangire Nyumba Yehova Mulungu wa Israeli. Onani mutuwo |