2 Mbiri 6:4 - Buku Lopatulika4 Nati iye, Alemekezedwe Yehova Mulungu wa Israele, wakunena m'kamwa mwake ndi Davide atate wanga, nakwaniritsa ndi manja ake, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Nati iye, Alemekezedwe Yehova Mulungu wa Israele, wakunena m'kamwa mwake ndi Davide atate wanga, nakwaniritsa ndi manja ake, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndipo mfumuyo idati, “Atamandike Chauta, Mulungu wa Aisraele, amene wachitadi ndi dzanja lake zimene adaalonjeza ndi pakamwa pake kwa Davide bambo wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo inati, “Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli amene wachita ndi dzanja lake zimene analonjeza ndi pakamwa pake kwa Davide abambo anga. Pakuti Iye anati, Onani mutuwo |