2 Mbiri 6:34 - Buku Lopatulika34 Akatulukira kunkhondo anthu anu kuyambana ndi adani ao, kutsata njira iliyonse muwatumiza; nakapemphera kwa Inu kuloza kumzinda uwu munausankha, ndi nyumba iyi ndaimangira dzina lanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Akatulukira kunkhondo anthu anu kuyambana ndi adani ao, kutsata njira iliyonse muwatumiza; nakapemphera kwa Inu kuloza kumudzi uwu munausankha, ndi nyumba iyi ndaimangira dzina lanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 “Anthu anu akamapita ku nkhondo kukamenyana ndi adani ao, kulikonse kumene mungaŵatume, akapemphera kwa Inu choyang'ana ku mzinda uno umene Inu mudausankha, ndiponso ku Nyumba imene ndakumangiraniyi yomveketsa dzina lanu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 “Anthu akapita ku nkhondo kukamenyana ndi adani awo, kulikonse kumene mungawatume, ndipo akapemphera moyangʼana mzinda uno umene mwausankha ndi Nyumba yanu imene ndakumangirani, Onani mutuwo |