2 Mbiri 6:2 - Buku Lopatulika2 Koma ndakumangirani nyumba yokhalamo, malo okhazikika okhalamo Inu nthawi yosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma ndakumangirani nyumba yokhalamo, malo okhazikika okhalamo Inu nthawi yosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndiye ine ndakumangirani nyumba yaulemerero, malo oti muzikhalamo nthaŵi zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ine ndakumangirani Nyumba yokongola kwambiri, malo woti muzikhalamo mpaka muyaya.” Onani mutuwo |