2 Mbiri 6:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ndalongamo likasa, muli chipangano cha Yehova, anachichita ndi ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ndalongamo likasa, muli chipangano cha Yehova, anachichita ndi ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono m'menemo ndaikamo Bokosi lija m'mene muli mau a chipangano cha Chauta chimene adachita ndi Aisraele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mʼmenemo ndayikamo Bokosi la Chipangano, mmene muli pangano la Yehova limene anapangana ndi ana a Israeli.” Onani mutuwo |