2 Mbiri 6:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo Solomoni anati, Yehova anati kuti adzakhala mu mdima wandiweyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo Solomoni anati, Yehova anati kuti adzakhala mu mdima wandiweyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Solomoni adapemphera nati, “Inu Chauta, mudanena kuti mudzakhala mu mdima waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pamenepo Solomoni anati, “Yehova anati adzakhala mʼmitambo yakuda; Onani mutuwo |