Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 5:4 - Buku Lopatulika

4 Nadza akuluakulu onse a Israele, nanyamula likasalo Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Nadza akuluakulu onse a Israele, nanyamula likasalo Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono atsogoleri onse a Aisraele atabwera, Alevi adanyamula Bokosi lachipangano lija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Akuluakulu onse a Israeli atafika, Alevi ananyamula Bokosi la Chipangano,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 5:4
8 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu onse a Israele anadza, ansembe nanyamula likasa.


Pamenepo Davide anati, Sayenera ena kusenza likasa la Mulungu koma Alevi ndiwo; pakuti Yehova anawasankha iwo kusenza likasa la Mulungu, ndi kumtumikira Iye kosatha.


Ndipo anakwera nalo likasa, ndi chihema chokomanako, ndi zipangizo zonse zopatulika zinali m'chihemamo; izizo ansembe Alevi anakwera nazo.


Ndipo ansembe analowa nalo likasa la chipangano la Yehova kumalo kwake m'chipinda chamkati mwa Kachisi, m'malo opatulika kwambiri, pansi pa mapiko a akerubi.


Atatha Aroni ndi ana ake aamuna kuphimba malo opatulika, ndi zipangizo zake zonse za malo opatulika, pofuna kumuka am'chigono; atatero, ana a Kohati adze kuzinyamula; koma asakhudze zopatulikazo, kuti angafe. Zinthu izi ndizo akatundu a ana a Kohati m'chihema chokomanako.


Ndipo Yoswa anati kwa ansembe, Senzani likasa la chipangano, nimuoloke pamaso pa anthu. Nasenza iwo likasa la chipangano, natsogolera anthu.


Ndipo Yoswa mwana wa Nuni anaitana ansembe, nanena nao, Senzani likasa la chipangano, ndi ansembe asanu ndi awiri anyamule mphalasa zisanu ndi ziwiri zanyanga za nkhosa zamphongo, kutsogolera nazo likasa la Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa