2 Mbiri 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo amuna onse a Israele anasonkhana kwa mfumu kumadyerero anachitikawo, m'mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo amuna onse a Israele anasonkhana kwa mfumu kumadyerero anachitikawo, m'mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Aisraele onse adasonkhana pamaso pa mfumu nthaŵi ya chikondwerero cha mwezi wachisanu ndi chiŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo Aisraeli onse anasonkhana pamaso pa mfumu nthawi ya chikondwerero cha mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwo |