2 Mbiri 4:22 - Buku Lopatulika22 ndi zozimira nyali, ndi mbale zowazira, ndi zipande, ndi mbale za zofukiza za golide woona; ndi kunena za polowera m'nyumba, zitseko zake za m'katimo za malo opatulika kwambiri, ndi zitseko za nyumbayi, ndiyo Kachisi, zinali zagolide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 ndi zozimira nyali, ndi mbale zowazira, ndi zipande, ndi mbale za zofukiza za golide woona; ndi kunena za polowera m'nyumba, zitseko zake za m'katimo za malo opatulika kwambiri, ndi zitseko za nyumbayi, ndiyo Kachisi, zinali zagolide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Zozimira nyale, mabeseni, mbale zofukiziramo lubani ndiponso ziwaya zopalira moto, zonsezi za golide weniweni. Ndipo adapangitsa zomangira zitseko za Nyumba ya Chauta ija, zitseko zam'kati zoloŵera ku malo opatulika kopambana, ndiponso zitseko zoloŵera m'Nyumba ya Chauta, zonsezo zinali zagolide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 zozimitsira nyale zagolide weniweni, mbale zowazira magazi, mbale ndi zofukizira; ndiponso zitseko zagolide za Nyumba ya Mulungu, chitseko cha ku Malo Opatulika Kwambiri ndi zitseko za ku chipinda chachikulu. Onani mutuwo |