2 Mbiri 4:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Solomoni anazipanga zipangizo izi zonse zochulukadi, pakuti kulemera kwake kwa mkuwa sikunayeseke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Solomoni anazipanga zipangizo izi zonse zochulukadi, pakuti kulemera kwake kwa mkuwa sikunayeseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Solomoni adapangitsa zinthu zimenezo zochuluka kwambiri, kotero kuti kulemera kwa mkuŵawo sikudadziŵike ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Zinthu zonse zimene Solomoni anapanga zinali zochuluka kwambiri kotero kuti kulemera kwa mkuwa sikunadziwike. Onani mutuwo |