2 Mbiri 4:16 - Buku Lopatulika16 Miphika yomwe, ndi zoolera, ndi mitungo, ndi zipangizo zake zonse, Huramuabi anazipangira mfumu Solomoni, kuzipangira nyumba ya Yehova, za mkuwa wonyezimira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Miphika yomwe, ndi zoolera, ndi mitungo, ndi zipangizo zake zonse, Huramuabi anazipangira mfumu Solomoni, kuzipangira nyumba ya Yehova, za mkuwa wonyezimira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mikhate, mafosholo, mafoloko ndiponso zipangizo zonse zofunikira pa zimenezi, Huramuabi adazipanga za mkuŵa wonyezemira, kupangira mfumu Solomoni ku Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Miphika, mafosholo, mafoloko otengera nyama ndi ziwiya zina zonse. Zipangizo zonse zimene Hiramu Abi anapangira Mfumu Solomoni za mʼNyumba ya Yehova zinali zamkuwa wonyezimira. Onani mutuwo |