Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 4:12 - Buku Lopatulika

12 nsanamira ziwiri, ndi zikhozo, ndi mitu iwiri inali pamwamba pa nsanamirazo, ndi maukonde awiri akukuta zikho ziwiri za mitu ili pamwamba pa nsanamirazo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 nsanamira ziwiri, ndi zikhozo, ndi mitu iwiri inali pamwamba pa nsanamirazo, ndi maukonde awiri akukuta zikho ziwiri za mitu ili pamwamba pa nsanamirazo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 ndiye kuti kumanga nsanamira ziŵiri zija, kupanga makapotolosi aŵiri aja okhala pamwamba pa nsanamirazo, ndiponso maukonde aŵiri aja ophimba ziwaya ziŵiri zija za kunsonga kwa makapotolosi aja okhala pamwamba pa nsanamira. Adapanganso maukonde aŵiri ovundikira pamwamba pa mbale ziŵiri za pa mitu imene inali pamwamba pa nsanamira ija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Nsanamira ziwiri; mbale ziwiri za mitu yapamwamba pa nsanamirazo; maukonde awiri okongoletsera mbale ziwiri za mitu yapamwamba pa nsanamirazo;

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 4:12
5 Mawu Ofanana  

Popeza iyeyu anaunda nsanamira ziwiri zamkuwa, msinkhu wake wa imodzi unali mikono khumi mphambu isanu ndi itatu; ndipo chingwe cha mikono khumi mphambu iwiri chinayesa thupi la nsanamira imodzi.


Nsanamira ziwirizo, ndi mbale za mitu inali pamwamba pa nsanamira ziwirizo, ndi maukonde awiri ophimbira mbale ziwiri za mitu inali pamwamba pa nsanamirazo,


Ndipo Huramu anapanga miphika, ndi zoolera zake, ndi mbale zowazira zake. Natsiriza Huramu ntchito adaichitira mfumu Solomoni m'nyumba ya Mulungu:


ndi makangaza mazana anai a maukonde awiriwa; mizere iwiri ya makangaza ya ukonde uliwonse, akukuta zikho ziwiri za mitu, inali pa nsanamirazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa