Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 4:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo Huramu anapanga miphika, ndi zoolera zake, ndi mbale zowazira zake. Natsiriza Huramu ntchito adaichitira mfumu Solomoni m'nyumba ya Mulungu:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Huramu anapanga miphika, ndi zoolera zake, ndi mbale zowazira zake. Natsiriza Huramu ntchito adaichitira mfumu Solomoni m'nyumba ya Mulungu:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Huramu adapanganso mikhate, mafosholo ndi mabeseni ambiri. Motero Huramu adamatsiriza ntchito ya Nyumba ya Chauta imene ankagwirira mfumu Solomoni:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Iye anapanganso miphika ndi mafosholo ndi mabeseni owazira magazi. Kotero Hiramu anatsiriza ntchito yonse ya ku Nyumba ya Mulungu imene ankagwirira Mfumu Solomoni:

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 4:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu Solomoni anatuma anthu kukatenga Hiramu ku Tiro.


Iyeyo anali mwana wake wa mkazi wamasiye wa fuko la Nafutali, atate wake anali munthu wa ku Tiro, mfundi wamkuwa; ndipo iye anadzala ndi nzeru ndi luntha ndi luso kugwira ntchito zonse za mkuwa. Ndipo anadza kwa mfumu Solomoni namgwirira ntchito zake zonse.


Ndi ku Tibati, ndi ku Kuni, mizinda ya Hadadezere, Davide anatenga mkuwa wambiri, ndiwo umene Solomoni anayenga nao thawale lamkuwa, ndi nsanamira, ndi zipangizo zamkuwa.


nsanamira ziwiri, ndi zikhozo, ndi mitu iwiri inali pamwamba pa nsanamirazo, ndi maukonde awiri akukuta zikho ziwiri za mitu ili pamwamba pa nsanamirazo,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa