2 Mbiri 32:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo analimbika mtima, namangitsa linga lonse mopasuka, nalikweza mpaka pansanja, ndi linga lina kunja kwake, nalimbitsa Milo m'mzinda wa Davide, napanga zida ndi zikopa zochuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo analimbika mtima, namangitsa linga lonse mopasuka, nalikweza mpaka pansanja, ndi linga lina kunja kwake, nalimbitsa Milo m'mudzi wa Davide, napanga zida ndi zikopa zochuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Hezekiya adalimba mtima, nayamba kumanganso khoma limene linali litagamuka. Tsono adamanganso nsanja pakhomapo, ndiponso ina kunja kwake. Adalimbitsanso linga lotchedwa Milo ku mzinda wa Davide. Adapanga zida zankhondo ndi zishango zambirimbiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kenaka iye anagwira ntchito molimbika kukonza madera ogumuka a khoma ndi kumangapo msanja. Anamanganso mpanda wina kunja kwa mpanda winawo ndipo anamanga zolimbitsa Milo ku mzinda wa Davide. Onani mutuwo |