2 Mbiri 32:4 - Buku Lopatulika4 Nasonkhana anthu ambiri, natseka akasupe onse, ndi mtsinje woyenda pakati padziko, ndi kuti, Angafike mafumu a Asiriya ndi kupeza madzi ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Nasonkhana anthu ambiri, natseka akasupe onse, ndi mtsinje woyenda pakati pa dziko, ndi kuti, Angafike mafumu a Asiriya ndi kupeza madzi ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 ndipo anthu ambiri adasonkhana kuti atseke akasupe onse pamodzi ndi mfuleni womwe umene unkayenda m'kati mwa nthakamo. Iwo ankati, “Akafika kuno mafumu a ku Asiriya, adzapezerenji madzi ambiri?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Gulu lalikulu la anthu linasonkhana, ndipo anatseka akasupe onse pamodzi ndi mtsinje umene umayenda mʼkati mwa nthakamo. Iwo ankanena kuti, “Nʼchifukwa chiyani mafumu a Asiriya akabwera kuno adzapeze madzi ambiri?” Onani mutuwo |