2 Mbiri 32:32 - Buku Lopatulika32 Machitidwe ena tsono a Hezekiya, ndi ntchito zake zokoma, taonani, zilembedwa m'masomphenya a Yesaya mneneri mwana wa Amozi, ndi m'buku la mafumu a Yuda ndi Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Machitidwe ena tsono a Hezekiya, ndi ntchito zake zokoma, taonani, zilembedwa m'masomphenya a Yesaya mneneri mwana wa Amozi, ndi m'buku la mafumu a Yuda ndi Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Tsono ntchito zonse za Hezekiya, pamodzi ndi zabwino zimene ankachita, zidalembedwa m'nkhani yosimba za zimene Yesaya mneneri mwana wa Amozi adaziwona m'masomphenya. Nkhani imeneyi idalembedwa m'buku la mafumu a ku Yuda ndi a ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Zina ndi zina zokhudza ulamuliro wa Hezekiya ndi ntchito za kudzipereka kwake zalembedwa mʼmasomphenya a Yesaya mwana wa Amozi, mʼbuku la mafumu a Yuda ndi Israeli. Onani mutuwo |