2 Mbiri 32:3 - Buku Lopatulika3 anapangana ndi akulu ake ndi amphamvu ake, kutseka madzi a mu akasupe okhala kunja kwa mzinda; namthandiza iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 anapangana ndi akulu ake ndi amphamvu ake, kutseka madzi a m'akasupe okhala kunja kwa mudzi; namthandiza iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 adapangana ndi nduna zake pamodzi ndi atsogoleri a gulu lankhondo, kuti akatseke madzi a ku akasupe kunja kwa mzindawo. Anthuwo adamthandiza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 iye anakambirana ndi akuluakulu ake pamodzi ndi atsogoleri a gulu lankhondo za kutseka akasupe ochoka ku kasupe amene anali kunja kwa mzinda, ndipo iwo anamuthandiza. Onani mutuwo |