2 Mbiri 32:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo pakuona Hezekiya kuti wadza Senakeribu, ndi kuti nkhope yake inalunjikitsa kuyambana nkhondo ndi Yerusalemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo pakuona Hezekiya kuti wadza Senakeribu, ndi kuti nkhope yake inalunjikitsa kuyambana nkhondo ndi Yerusalemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Hezekiya ataona kuti Senakeribu wabwera, ndipo akufuna kuthira nkhondo Yerusalemu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pamene Hezekiya anaona kuti Senakeribu wabwera ndipo wakonzeka kuchita nkhondo ndi Yerusalemu, Onani mutuwo |