2 Mbiri 32:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo anyamata ake anaonjeza kunena motsutsana ndi Yehova Mulungu, ndi mnyamata wake Hezekiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo anyamata ake anaonjeza kunena motsutsana ndi Yehova Mulungu, ndi mnyamata wake Hezekiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Akazembe akewo ankalankhula zambiri zonyoza Ambuye Chauta ndi mtumiki wake Hezekiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Atsogoleri a ankhondo a Senakeribu anapitiriza kuyankhula zotsutsana ndi Yehova Mulungu ndi mtumiki wake Hezekiya. Onani mutuwo |