Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 32:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anyamata ake anaonjeza kunena motsutsana ndi Yehova Mulungu, ndi mnyamata wake Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anyamata ake anaonjeza kunena motsutsana ndi Yehova Mulungu, ndi mnyamata wake Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Akazembe akewo ankalankhula zambiri zonyoza Ambuye Chauta ndi mtumiki wake Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Atsogoleri a ankhondo a Senakeribu anapitiriza kuyankhula zotsutsana ndi Yehova Mulungu ndi mtumiki wake Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 32:16
5 Mawu Ofanana  

Ndipo tsono, asakunyengeni Hezekiya, ndi kukukopani motero, musamkhulupirira; pakuti palibe Mulungu wa mtundu uliwonse wa anthu, kapena ufumu uliwonse, unakhoza kulanditsa anthu ake m'dzanja mwanga; ndipo kodi Mulungu wanu adzakulanditsani inu m'dzanja langa?


Analemberanso makalata a kunyoza Yehova Mulungu wa Israele, ndi kunena motsutsana ndi Iye, ndi kuti, Monga milungu ya mitundu ya anthu a m'maiko, imene siinalanditse anthu ao m'dzanja langa, momwemo Mulungu wa Hezekiya sadzalanditsa anthu ake m'dzanja mwanga.


Pakamwa pao anena zam'mwamba, ndipo lilime lao liyendayenda m'dziko lapansi.


Koma izi zonse adzakuchitirani chifukwa cha dzina langa, chifukwa sadziwa wondituma Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa