2 Mbiri 32:13 - Buku Lopatulika13 Simudziwa kodi chomwe ine ndi makolo anga tachitira anthu onse a m'maikomo? Kodi milungu ya mitundu ya anthu inakhoza konse kulanditsa dziko lao m'dzanja langa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Simudziwa kodi chomwe ine ndi makolo anga tachitira anthu onse a m'maikomo? Kodi milungu ya mitundu ya anthu inakhoza konse kulanditsa dziko lao m'dzanja langa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kodi inu simukudziŵa zimene ine ndi makolo anga takhala tikuichita mitundu yonse ya anthu a maiko ena? Kodi milungu ya mitundu ina ya anthu a m'maikowo idatha kupulumutsa maiko ao m'manja mwanga? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Kodi inu simukudziwa zimene ine ndi makolo anga tachita kwa anthu a mitundu ina? Kodi milungu ya mitundu imeneyi inatha kupulumutsa dziko lawo kuchoka mʼdzanja langa? Onani mutuwo |