2 Mbiri 32:10 - Buku Lopatulika10 Atero Senakeribu mfumu ya Asiriya, Mutama chiyani kuti mukhala m'linga mu Yerusalemu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Atero Senakeribu mfumu ya Asiriya, Mutama chiyani kuti mukhala m'linga m'Yerusalemu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Senakeribu, mfumu ya ku Asiriya, akufunsa kuti, ‘Kodi mukukhulupirira chiyani, kuti muzikanirira mu Yerusalemu ndi kumatsekedwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Senakeribu mfumu ya ku Asiriya akuti: Kodi inu mukukhulupirira chiyani, kuti mukukhalabe mu Yerusalemu mutazingidwa? Onani mutuwo |