2 Mbiri 30:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti mfumu idapangana ndi akulu ake, ndi msonkhano wonse wa mu Yerusalemu, kuti achite Paska mwezi wachiwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti mfumu idapangana ndi akulu ake, ndi msonkhano wonse wa m'Yerusalemu, kuti achite Paska mwezi wachiwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pakuti mfumu, nduna zake ndi anthu onse a ku Yerusalemu anali atapangana kuti azichita Paska pa mwezi wachiŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mfumu ndi akuluakulu ake pamodzi ndi anthu onse a mu Yerusalemu anagwirizana kuti akondwerere Paska pa mwezi wachiwiri. Onani mutuwo |