Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 3:9 - Buku Lopatulika

9 Ndi kulemera kwake kwa misomali ndiko masekeli makumi asanu a golide. Ndipo anazikuta ndi golide zipinda zosanjikizana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndi kulemera kwake kwa misomali ndiko masekeli makumi asanu a golide. Ndipo anazikuta ndi golide zipinda zosanjikizana.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Magaramu 570 a golide adaŵagwiritsa ntchito kupanga misomali. Ndipo zipinda zapamwamba adazikutanso ndi golide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Misomali yagolide imalemera magalamu 570. Anakutanso ndi golide zipinda zapamwamba.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 3:9
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide anapatsa Solomoni mwana wake chifaniziro cha chipinda cholowera cha Kachisi, ndi cha nyumba zake, ndi cha zosungiramo chuma zake, ndi cha zipinda zosanjikizana zake, ndi cha zipinda zake za m'katimo, ndi cha Kachisi wotetezerepo;


Ndipo m'malo opatulika kwambiri anapanga akerubi awiri, anachita osema, nawakuta ndi golide.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa