Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 3:7 - Buku Lopatulika

7 Anamamatizanso Kachisi, mitanda, ziundo, ndi makoma ake, ndi zitseko zake, ndi golide; nalemba akerubi pamakoma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Anamamatizanso Kachisi, mitanda, ziundo, ndi makoma ake, ndi zitseko zake, ndi golide; nalemba akerubi pamakoma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Motero adaikuta nyumba yonseyo ndi golide, ndiye kuti mitanda yake, ziwundo zake, makoma ake ndi zitseko zake zomwe. Ndipo adazokota zithunzi za akerubi pa makoma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iye anakutira ndi golide mitanda ya ku denga, maferemu a zitseko, makoma ndi zitseko za Nyumba ya Mulungu, ndipo anajambula Akerubi mʼmakoma mwake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 3:7
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anakuta nyumba ndi miyala ya mtengo wake; ndi golide wake ndiye golide wa Paravaimu.


Ndipo uzipanga chihema ndi nsalu zophimba khumi, za bafuta wa thonje losansitsa, ndi thonje lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira; uombemo akerubi, ntchito ya mmisiri.


Ndipo uzikuta matabwa ndi golide, ndi kupanga mphete zao zagolide zopisamo mitandayo; uzikutanso mitandayo ndi golide.


Ndipo chokometsera chake chokongola anachiyesa chodzikuza nacho, napangira mafanizo olaula, ndi zonyansa zao zina; chifukwa chake ndinapatsa ichi chikhale chowadetsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa