Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 3:5 - Buku Lopatulika

5 M'nyumba yaikulu tsono anatchinga ndi mitengo yamlombwa, imene anaikuta ndi golide wabwino, nalembapo ngati migwalangwa ndi maunyolo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 M'nyumba yaikulu tsono anatchinga ndi mitengo yamlombwa, imene anaikuta ndi golide wabwino, nalembapo ngati migwalangwa ndi maunyolo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Chipinda chachikulucho adachichinga ndi matabwa amlombwa, nachikuta ndi golide wosalala, ndipo pamakoma adalochapo zithunzi za kanjedza ndi za maunyolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Chipinda chachikulu, khoma lake anakhomera matabwa a payini ndipo analikutira ndi golide wabwino ndi kulikongoletsa ndi zithunzi za kanjedza ndi maunyolo.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 3:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anakuta nyumba ndi miyala ya mtengo wake; ndi golide wake ndiye golide wa Paravaimu.


Mitanda ya nyumba zathu nja mikungudza, ndi mapaso athu nga mlombwa.


Ndipo panali mazenera amkati okhazikika pazipinda ndi m'makoma a pakati pao, m'kati mwa chipata pozungulira ponse; momwemonso pamphuthu; ndipo panali mazenera pozungulira ponse m'katimo, ndi pa nsanamirazo panali akanjedza.


Ndipo panalembedwapo ndi akerubi ndi akanjedza, kanjedza pakati pa akerubi; ndi kerubi aliyense anali ndi nkhope zake ziwiri;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa