2 Mbiri 3:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo maziko adawaika Solomoni akumangapo nyumba ya Mulungu ndi awa: utali wake, kuyesa mikono monga mwa muyeso wakale, ndiwo mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo maziko adawaika Solomoni akumangapo nyumba ya Mulungu ndi awa: utali wake, kuyesa mikono monga mwa muyeso wakale, ndiwo mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nyumba ya Chautayo, miyeso yake imene Solomoni adaapereka inali iyi: Potsata miyeso yakale, m'litali mwake inali ya mamita 27, ndipo m'mimba mwake inali ya mamita asanu ndi anai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Maziko amene Solomoni anayika pomanga Nyumba ya Mulungu ndi awa: Mulitali munali mamita 27, mulifupi munali mamita asanu ndi anayi (potsata miyeso yakale). Onani mutuwo |