Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 27:8 - Buku Lopatulika

8 Anali wa zaka makumi awiri mphambu zisanu polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Anali wa zaka makumi awiri mphambu zisanu polowa ufumu wake, nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Iyeyo anali wa zaka 25 pamene ankaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 16 ku Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iye anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 27:8
2 Mawu Ofanana  

Yotamu anali wa zaka makumi awiri, mphambu zisanu polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka khumi ndi zisanu ndi chimodzi; ndi dzina la make ndiye Yerusa mwana wa Zadoki.


Ndipo Yotamu anagona ndi makolo ake, namuika m'mzinda wa Davide; ndi Ahazi mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa