2 Mbiri 27:6 - Buku Lopatulika6 Momwemo Yotamu anakula mphamvu, popeza anakonza njira zake pamaso pa Yehova Mulungu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Momwemo Yotamu anakula mphamvu, popeza anakonza njira zake pamaso pa Yehova Mulungu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Choncho Yotamu adasanduka wamphamvu chifukwa chakuti adasunga makhalidwe oongoka pamaso pa Chauta Mulungu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yotamu anakula mphamvu chifukwa anayenda molungama pamaso pa Yehova Mulungu wake. Onani mutuwo |