Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 27:6 - Buku Lopatulika

6 Momwemo Yotamu anakula mphamvu, popeza anakonza njira zake pamaso pa Yehova Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Momwemo Yotamu anakula mphamvu, popeza anakonza njira zake pamaso pa Yehova Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Choncho Yotamu adasanduka wamphamvu chifukwa chakuti adasunga makhalidwe oongoka pamaso pa Chauta Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Yotamu anakula mphamvu chifukwa anayenda molungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 27:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anali ndi Yehosafati, popeza anayenda m'njira zake zoyamba za kholo lake Davide, osafuna Abaala;


koma anafuna Mulungu wa kholo lake nayenda m'malamulo ake, osatsata machitidwe a Israele.


Koma zapezeka zokoma mwa inu, popeza mwazichotsa zifanizo m'dzikomo, mwalunjikitsanso mtima wanu kufuna Mulungu.


Ndipo iye anali munthu wakufuna Mulungu masiku a Zekariya, ndiye wozindikira masomphenya a Mulungu; ndipo masiku akufunira Yehova iye, Mulungu anamlemereza;


Anayambananso ndi mfumu ya ana a Amoni, namgonjetsa. Ndi ana a Amoni anamninkha chaka chomwechi matalente a siliva zana limodzi, ndi miyeso ya tirigu zikwi khumi, ndi ya barele zikwi khumi. Ana a Amoni anabwera nazo zomwezo kwa iye chaka chachiwiri ndi chachitatu chomwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa