Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 27:4 - Buku Lopatulika

4 Namanga mizinda m'mapiri a Yuda, ndi m'nkhalango anamanga nyumba zansanja, ndi nsanja zomwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Namanga midzi m'mapiri a Yuda, ndi m'nkhalango anamanga nyumba zansanja, ndi nsanja zomwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Komanso adamanga mizinda ku dziko lonse lamapiri la Yuda. Adamanganso malinga ndi nsanja ku nkhalango zakumapiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Iye anamanga mizinda mʼmapiri a ku Yuda ndipo anamanganso malinga ndi nsanja mʼmadera a ku nkhalango.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 27:4
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa Yuda, Timange mizinda iyi ndi kuizingira malinga, ndi nsanja, zitseko, ndi mipiringidzo; dziko likali pamaso pathu, popeza tafuna Yehova Mulungu wathu; tamfuna Iye, natipatsa mpumulo pozungulira ponse. Momwemo anamanga mosavutika.


Ndipo Yehosafati anakula chikulire, namanga mu Yuda nyumba zansanja, ndi mizinda ya chuma.


Anayambananso ndi mfumu ya ana a Amoni, namgonjetsa. Ndi ana a Amoni anamninkha chaka chomwechi matalente a siliva zana limodzi, ndi miyeso ya tirigu zikwi khumi, ndi ya barele zikwi khumi. Ana a Amoni anabwera nazo zomwezo kwa iye chaka chachiwiri ndi chachitatu chomwe.


Ndipo Maria ananyamuka masiku amenewa, namuka ndi changu kudziko la mapiri kumzinda wa Yuda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa