Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 27:3 - Buku Lopatulika

3 Anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova, ndi pa linga la Ofele anamanga kwakukulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova, ndi pa linga la Ofele anamanga kwakukulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Iyeyo adamanga khomo lapamwamba la ku Nyumba ya Chauta, ndipo adagwira ntchito yaikulu yomanga linga la Ofele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Yotamu anamanganso chipata chakumtunda cha Nyumba ya Yehova ndipo anagwira ntchito yayikulu yomanga khoma la ku phiri la Ofeli.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 27:3
6 Mawu Ofanana  

Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje. Iye anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova.


Natenga atsogoleri a mazana, ndi omveka, ndi akazembe a anthu, ndi anthu onse a m'dziko, natsika ndi mfumu kunyumba ya Yehova; nalowera pa chipata cha kumtunda m'nyumba ya mfumu, namkhalitsa mfumu pa mpando wa ufumu.


Chitatha ichi tsono iye anaumangira mzinda wa Davide linga lakunja, kumadzulo kwa Gihoni, m'chigwa, mpaka polowera pa Chipata cha Nsomba; nazinga Ofele, nalikweza kwambiri; anaikanso akazembe a nkhondo m'mizinda yonse yamalinga ya mu Yuda.


Ndipo Pasuri anampanda Yeremiya mneneriyo, namuika matangadza amene anali mu Chipata cha Benjamini cha kumtunda, chimene chinali kunyumba ya Yehova.


Ndipo pamene akulu a Yuda anamva zimenezi, anakwera kutuluka kunyumba ya mfumu kunka kunyumba ya Yehova; ndipo anakhala pa khomo la Chipata Chatsopano cha nyumba ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa