2 Mbiri 27:3 - Buku Lopatulika3 Anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova, ndi pa linga la Ofele anamanga kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova, ndi pa linga la Ofele anamanga kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iyeyo adamanga khomo lapamwamba la ku Nyumba ya Chauta, ndipo adagwira ntchito yaikulu yomanga linga la Ofele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yotamu anamanganso chipata chakumtunda cha Nyumba ya Yehova ndipo anagwira ntchito yayikulu yomanga khoma la ku phiri la Ofeli. Onani mutuwo |