Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 27:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo adachitira atate wake Uziya; pokhapo sanalowe mu Kachisi wa Yehova. Koma anthu anachitabe zovunda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo adachitira atate wake Uziya; pokhapo sanalowe m'Kachisi wa Yehova. Koma anthu anachitabe zovunda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Iyeyo adachita zolungama pamaso pa Chauta, kutsata zonse zimene ankachita Uziya, bambo wake, kupatula kuti sadakaloŵe mwamphamvu ku Nyumba ya Chauta. Koma anthu ankachitabe zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga anachitira Uziya abambo ake, kupatula kuti iyeyo sanalowe mʼNyumba ya Yehova. Komabe anthu anapitirira kuchita zoyipa.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 27:2
8 Mawu Ofanana  

Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.


Ahazi anali wa zaka makumi awiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi; koma sanachite zoongoka pamaso pa Yehova ngati Davide kholo lake,


Thupi langa linjenjemera ndi kuopa Inu; ndipo ndichita mantha nao maweruzo anu.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Muka, tsikatu, pakuti anthu ako udakwera nao kuchokera m'dziko la Ejipito wadziipsa;


Mtundu wochimwa inu, anthu olemedwa ndi mphulupulu, mbeu yakuchita zoipa, ana amene achita moononga, iwo amsiya Yehova, iwo amnyoza Woyera wa Israele, iwo adana naye nabwerera m'mbuyo.


Koma palibe mmodzi wa otsalawo analimba mtima kuphatikana nao; komatu anthu anawakuzitsa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa