2 Mbiri 26:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Aamoni anampatsa Uziya mitulo; ndi dzina lake linabuka mpaka polowera ku Ejipito; pakuti analimbika chilimbikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Aamoni anampatsa Uziya mitulo; ndi dzina lake linabuka mpaka polowera ku Ejipito; pakuti analimbika chilimbikire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Aamoni ankakhoma msonkho kwa Uziya, ndipo mbiri yake idamveka mpaka ku malire a Ejipito, poti anali wamphamvu kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Aamoni ankabweretsa msonkho kwa Uziya ndipo mbiri yake inamveka mpaka ku malire a dziko la Igupto chifukwa anali wamphamvu kwambiri. Onani mutuwo |