2 Mbiri 26:4 - Buku Lopatulika4 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adachita zolungama pamaso pa Chauta, monga momwe ankachitira bambo wake Amaziya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Amaziya abambo ake. Onani mutuwo |