Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 26:4 - Buku Lopatulika

4 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Adachita zolungama pamaso pa Chauta, monga momwe ankachitira bambo wake Amaziya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Amaziya abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 26:4
8 Mawu Ofanana  

Anali wa zaka khumi ndi zisanu ndi chimodzi polowa ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi asanu mphambu ziwiri mu Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Yekoliya wa ku Yerusalemu.


Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova; anachita monga mwa zonse anazichita atate wake Uziya.


Ndipo Yowasi anachita zoongoka pamaso pa Yehova masiku onse a Yehoyada wansembe.


Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, koma wosachita ndi mtima wangwiro.


Uziya anali wa zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi asanu mphambu ziwiri; ndi dzina la make ndiye Yekoliya wa ku Yerusalemu.


Ndipo iye anali munthu wakufuna Mulungu masiku a Zekariya, ndiye wozindikira masomphenya a Mulungu; ndipo masiku akufunira Yehova iye, Mulungu anamlemereza;


Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo adachitira atate wake Uziya; pokhapo sanalowe mu Kachisi wa Yehova. Koma anthu anachitabe zovunda.


Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo monse adachitira Davide kholo lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa