2 Mbiri 26:22 - Buku Lopatulika22 Machitidwe ena tsono a Uziya, oyamba ndi otsiriza, anawalemba Yesaya mneneri mwana wa Amozi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Machitidwe ena tsono a Uziya, oyamba ndi otsiriza, anawalemba Yesaya mneneri mwana wa Amozi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ntchito zonse za Uziya kuyambira pa chiyambi mpaka pomaliza, adazilemba mneneri Yesaya, mwana wa Amozi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ntchito zina za mfumu Uziya, kuyambira pachiyambi mpaka pa mapeto, zinalembedwa ndi mneneri Yesaya mwana wa Amozi. Onani mutuwo |