2 Mbiri 26:2 - Buku Lopatulika2 Iye anamanga Eloti, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Iye anamanga Eloti, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyeyo adamanga mzinda wa Eloti naubwezera ku Yuda, mfumu itamwalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anamanganso mzinda wa Eloti ndi kuwubwezeranso ku Yuda abambo ake atamwalira. Onani mutuwo |