Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 26:2 - Buku Lopatulika

2 Iye anamanga Eloti, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Iye anamanga Eloti, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Iyeyo adamanga mzinda wa Eloti naubwezera ku Yuda, mfumu itamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anamanganso mzinda wa Eloti ndi kuwubwezeranso ku Yuda abambo ake atamwalira.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 26:2
7 Mawu Ofanana  

Anamanga Elati, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake.


Nthawi yomweyo Rezini mfumu ya Aramu anabwezera Elati kwa Aramu, napirikitsa Ayuda ku Elati; nadza Aaramu ku Elati, nakhala komwemo kufikira lero lino.


Ndipo Yowasi mfumu ya Israele anagwira Amaziya mfumu ya Yuda, mwana wa Yowasi mwana wa Yehowahazi, ku Betesemesi, nabwera naye ku Yerusalemu, nagamula linga la Yerusalemu kuyambira Chipata cha Efuremu kufikira Chipata cha Kungodya, mikono mazana anai.


Namnyamula pa akavalo, namuika pamodzi ndi makolo ake m'mzinda wa Yuda.


Ndipo anthu onse Ayuda anatenga Uziya, ndiye wa zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi, namlonga ufumu m'malo mwa atate wake Amaziya.


Uziya anali wa zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi asanu mphambu ziwiri; ndi dzina la make ndiye Yekoliya wa ku Yerusalemu.


Pamenepo Solomoni anamuka ku Eziyoni-Gebere, ndi ku Eloti m'mphepete mwa nyanja, m'dziko la Edomu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa