Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 26:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Azariya wansembe analowa pambuyo pake, ndi pamodzi naye ansembe a Yehova makumi asanu ndi atatu, ndiwo olimba mtima;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Azariya wansembe analowa pambuyo pake, ndi pamodzi naye ansembe a Yehova makumi asanu ndi atatu, ndiwo olimba mtima;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Koma wansembe Azariya adaloŵa pambuyo pa iyeyo, pamodzi ndi ansembe a Chauta 80 olimba mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Wansembe Azariya pamodzi ndi ansembe a Yehova ena 80 olimba mtima anamutsatira.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 26:17
4 Mawu Ofanana  

ndi Zadoki, ndiye mnyamata, ngwazi yamphamvu, ndi a nyumba ya kholo lake akulu makumi awiri mphambu awiri.


Kwa Semaya mwana wake yemwe kunabadwa ana, akulamulira nyumba ya atate wao; pakuti anali ngwazi zamphamvu.


ndi Yohanani anabala Azariya (ndiye amene anachita ntchito ya nsembe m'nyumba anaimanga Solomoni mu Yerusalemu),


natsutsana ndi mfumu Uziya, nati kwa iye, Sikuyenera inu, Uziya, kufukizira Yehova koma ansembe, ana a Aroni opatulidwira kufukiza; tulukani m'malo opatulika; pakuti mwalakwa; Yehova Mulungu sakulemekezanipo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa