2 Mbiri 26:12 - Buku Lopatulika12 Chiwerengo chonse cha akulu a nyumba za makolo, ndiwo ngwazi zamphamvu, ndicho zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Chiwerengo chonse cha akulu a nyumba za makolo, ndiwo ngwazi zamphamvu, ndicho zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chiŵerengero chonse cha atsogoleri amphamvu, olimba mtima, akulu a mabanja, chinali 2,600. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Chiwerengero chonse cha atsogoleri a mʼmabanja oyangʼanira anthu ochita nkhondo chinali 2,600. Onani mutuwo |