2 Mbiri 25:3 - Buku Lopatulika3 Kunachitika tsono, utamkhazikikira ufumu, anapha anyamata ake amene adapha mfumu atate wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kunachitika tsono, utamkhazikikira ufumu, anapha anyamata ake amene adapha mfumu atate wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono atangolandira mphamvu zonse zaufumu m'manja mwake, adapha anyamata ake amene adaapha mfumu ija, bambo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene mphamvu zonse zaufumu zinali mʼmanja mwake, iye anapha akuluakulu amene anapha abambo ake, mfumu ija. Onani mutuwo |