2 Mbiri 24:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo pambuyo pake mumtima mwa Yowasi munali chofuna kukonzanso nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo pambuyo pake mumtima mwa Yowasi munali chofuna kukonzanso nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pambuyo pake Yowasi adatsimikiza zokonzanso Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Patapita nthawi Yowasi anatsimikiza zokonzanso Nyumba ya Yehova. Onani mutuwo |