2 Mbiri 24:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yehoyada anamtengera akazi awiri, nabala ana aamuna ndi aakazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yehoyada anamtengera akazi awiri, nabala ana aamuna ndi aakazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yehoyada adaipezera mfumuyo akazi aŵiri, ndipo idabereka ana aamuna ndi ana aakazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yehoyada anamupezera iye akazi awiri, ndipo anabereka ana aamuna ndi aakazi. Onani mutuwo |