Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 24:1 - Buku Lopatulika

1 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la make ndiye Zibiya wa ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la make ndiye Zibiya wa ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziŵiri pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 40 ku Yerusalemu. Mai wake anali Zibiya wa ku Beereseba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri pamene anakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka makumi anayi. Dzina la amayi ake linali Zibiya wa ku Beeriseba.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 24:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa, natenga mkate ndi thumba la madzi, nampatsa Hagara, naika paphewa pake, ndi mwana, namchotsa iye: ndipo iye anamuka, nasocherera m'chipululu cha Beereseba.


Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa iye ufumu.


Chaka chachisanu ndi chiwiri cha Yehu, Yowasi analowa ufumu wake; nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mai wake ndiye Zibiya wa ku Beereseba.


Yoramu mwana wake, Ahaziya mwana wake, Yowasi mwana wake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa