Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 22:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo kunali, pakulanga Yehu nyumba ya Ahabu, anapeza akalonga a Yuda, ndi ana a abale a Ahaziya, akutumikira Ahaziya, nawapha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo kunali, pakulanga Yehu nyumba ya Ahabu, anapeza akalonga a Yuda, ndi ana a abale a Ahaziya, akutumikira Ahaziya, nawapha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Pamene Yehu ankalanga banja la Ahabu lija, adakumana ndi atsogoleri a ku Yuda ndiponso ana aamuna a abale ake a Ahaziya, amene ankatumikira Ahaziya, iye nkuŵapha onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pamene Yehu ankalanga banja la Ahabu anapeza atsogoleri a ku Yuda ndiponso ana aamuna a abale ake a Ahaziya amene amatumikira Ahaziya, ndipo anawapha.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 22:8
2 Mawu Ofanana  

Pakuti khamu la nkhondo la Aaramu linadza la anthu owerengeka; ndipo Yehova anapereka khamu lalikulu m'dzanja lao; popeza adasiya Yehova Mulungu wa makolo ao. Motero anachitira Yowasi zomlanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa