2 Mbiri 22:3 - Buku Lopatulika3 Iyenso anayenda m'njira za nyumba ya Ahabu; pakuti wompangira ndi make achite choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Iyenso anayenda m'njira za nyumba ya Ahabu; pakuti wompangira ndi make achite choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iyeyonso ankatsata chitsanzo cha banja la Ahabu, poti mai wake ndiye ankamupatsa uphungu woipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nayenso anayenda mʼnjira ya banja la Ahabu, pakuti amayi ake anamulimbikitsa kuchita zolakwika. Onani mutuwo |