2 Mbiri 22:2 - Buku Lopatulika2 Ahaziya anali wa zaka makumi anai mphambu ziwiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu chaka chimodzi; ndi dzina la make ndiye Ataliya mwana wa Omuri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ahaziya anali wa zaka makumi anai mphambu ziwiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu m'Yerusalemu chaka chimodzi; ndi dzina la make ndiye Ataliya mwana wa Omuri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ahaziyayo anali wa zaka 42 pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira chaka chimodzi ku Yerusalemu. Mai wake anali Ataliya, mdzukulu wake wa Omuri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ahaziya anali wa zaka 22 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu chaka chimodzi. Dzina la amayi ake linali Ataliya, chidzukulu cha Omuri. Onani mutuwo |