Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 21:5 - Buku Lopatulika

5 Yehoramu anali wa zaka makumi atatu mphambu ziwiri polowa ufumu wake, nachita ufumu mu Yerusalemu zaka zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Yehoramu anali wa zaka makumi atatu mphambu ziwiri polowa ufumu wake, nachita ufumu m'Yerusalemu zaka zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Yehoramu anali wa zaka 32 pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka zisanu ndi zitatu ku Yerusalemu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Yehoramu anali wa zaka 32 pamene anakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 21:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza ziwiri, nabala Serugi:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa