2 Mbiri 21:4 - Buku Lopatulika4 Atauka tsono Yehoramu mu ufumu wa atate wake, nadzilimbitsa, anapha ndi lupanga abale ake onse, ndi akalonga ena omwe a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Atauka tsono Yehoramu m'ufumu wa atate wake, nadzilimbitsa, anapha ndi lupanga abale ake onse, ndi akalonga ena omwe a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yehoramu ataloŵa ufumu, nakhazikika pa mpando waufumu wa atate akewo, adapha abale ake onse ndi lupanga, ngakhalenso atsogoleri ena a ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehoramu atakhazikika pa ufumu wa abambo ake, iye anapha abale ake ndi lupanga pamodzi ndi atsogoleri ena a Israeli. Onani mutuwo |