Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 21:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehosafati anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake m'mzinda wa Davide; ndi Yehoramu mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehosafati anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake m'mudzi wa Davide; ndi Yehoramu mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Yehosafati adamwalira, naikidwa m'manda momwe adaaikidwa makolo akewo mu mzinda wa Davide. Tsono Yehoramu mwana wake adaloŵa ufumu m'malo mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehosafati anamwalira nayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake mu mzinda wa Davide. Ndipo Yehoramu mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 21:1
8 Mawu Ofanana  

Ndipo ananyamula Asahele namuika m'manda a atate wake ali ku Betelehemu. Ndipo Yowabu ndi anthu ake anachezera kuyenda usiku wonse, ndipo kudawachera ku Hebroni.


Ndipo Yehosafati anagona ndi makolo ake, naikidwa ndi makolo ake m'mzinda wa Davide kholo lake; ndipo Yehoramu mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Nagona Yoramu ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake m'mzinda wa Davide; ndipo Ahaziya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Nagona Rehobowamu ndi makolo ake, naikidwa m'mzinda wa Davide; ndipo Abiya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Pamenepo Eliyezere mwana wa Dodavahu wa Maresa ananenera kumtsutsa Yehosafati, ndi kuti, Popeza waphatikana ndi Ahaziya Yehova wapasula ntchito zako. Ndipo zombo zinasweka zosakhoza kumuka ku Tarisisi.


Anali wa zaka makumi atatu mphambu ziwiri polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka zisanu ndi zitatu, namuka wopanda wina womlakalaka; ndipo anamuika m'mzinda wa Davide, koma si m'manda a mafumu ai.


Nagona Solomoni pamodzi ndi makolo ake, naikidwa m'mzinda wa Davide atate wake; ndipo Rehobowamu mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa