2 Mbiri 20:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yehosafati anachita mantha, nalunjikitsa nkhope yake kufuna Yehova, nalalikira kusala mwa Ayuda onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yehosafati anachita mantha, nalunjikitsa nkhope yake kufuna Yehova, nalalikira kusala mwa Ayuda onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamenepo Yehosafati adachita mantha, ndipo adaganiza zopempha nzeru kwa Chauta, nalengeza kuti anthu onse a ku dziko la Yuda asale zakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndi mantha, Yehosafati anaganiza zofunsira kwa Yehova, ndipo analengeza kuti Ayuda onse asale zakudya. Onani mutuwo |